The Children's Questions about Faith

 

This book is directed to Muslim parents devoted in teaching faith to their children in the times of globalization and unlimited access through technology to all that is confusing and/or contradictory to the Islamic faith.

This book is divided into two sections, the first section provides parents with the most important faith related information they need to teach their kids. The second part provides parents with ways to respond to questions children might ask about faith. Both sections complement one another.

 

MAFUNSO A ANA pA CHIKHULUPILIRO

 

Bukuli lagawidwa m’magawo awiri : gawo loyamba (zokhudza maphunziro

a chikhulupiliro ), m’menemo muli maziko ambiri omwe angathandize

makolo kuphunzitsa ana awo – mu chifuniro cha Allah -,

pomwe gawo la chiwiri likuzungulira pa (zitsanzo zochitika pakayankhidwe

ka mafunso a ana okhudza chikhululupiliro) m’menemo tiyankhamo

mafunso amene ali otchuka kwambiri pakati pa ana amisinkhu yosiyana

siyana, makamaka omwe akukhudzana ndi msichi zachikhulupiliro

zisanu ndi imodzi (6) ndipo tafotokozamo momveka bwino m’mene tingayankhire

mafunso ngati amenewa

You may also enjoy